Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 50:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Pakuti nyama iliyonse yakutchire ndi yanga,+

      Ndiponso nyama zopezeka m’mapiri 1,000.+

  • Salimo 51:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 Pakuti nsembe singakusangalatseni, chifukwa ikanakusangalatsani ndikanaipereka kwa inu.+

      Nsembe yopsereza yathunthu singakusangalatseni.+

  • Ezekieli 16:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Unali kutenganso zovala zako za nsalu yopeta n’kuphimbira zifanizirozo. Komanso unkaika mafuta anga ndi zonunkhiritsa zanga+ pamaso pa zifanizirozo.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena