Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 119:120
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 120 Chifukwa choopa inu, thupi langa linagwidwa nthumanzi,+

      Ndipo chifukwa cha zigamulo zanu, ndinachita mantha.+

  • Yeremiya 23:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 Mtima wanga wasweka mkati mwanga chifukwa cha aneneri. Mafupa anga onse ayamba kunjenjemera. Ndakhala ngati munthu woledzera,+ komanso mwamuna wamphamvu amene wagonjetsedwa ndi vinyo, chifukwa cha Yehova komanso chifukwa cha mawu ake oyera.

  • Danieli 8:27
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 27 Ndiyeno ineyo Danieli ndinatopa kwambiri ndipo ndinadwala kwa masiku angapo.+ Kenako ndinadzuka ndi kugwira ntchito yotumikira mfumu.+ Koma ndinali wodabwa kwambiri ndi zimene ndinaona, ndipo palibe amene anazimvetsa.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena