Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 21:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  5 Ulemerero wake ndi waukulu m’chipulumutso chanu.+

      Mwaipatsa ulemu ndi ulemerero.+

  • Salimo 45:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  3 Mangirira lupanga lako+ m’chiuno mwako wamphamvu iwe,+

      Limodzi ndi ulemu ndiponso ulemerero wako.+

  • Yesaya 22:24
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 24 Anthu adzapachika pa iyeyo ulemerero wonse wa nyumba ya bambo ake: mbadwa ndi mphukira, kutanthauza mitundu yonse ya ziwiya zing’onozing’ono, mitundu yonse ya ziwiya zolowa, ndi mitundu yonse ya mitsuko ikuluikulu.’

  • Aheberi 5:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 Zilinso chimodzimodzi ndi Khristu. Iye sanadzipatse yekha ulemerero+ mwa kudziika yekha kukhala mkulu wa ansembe.+ Koma amene anamupatsa+ ulemerero umenewo ndi amene analankhula zokhudza iyeyu kuti: “Iwe ndiwe mwana wanga. Lero ine ndakhala atate wako.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena