Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 36:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  4 Ali pabedi lake amakonza chiwembu kuti apweteke anzake.+

      Amaima panjira yoipa.+

      Sapewa kuchita zinthu zoipa.+

  • Miyambo 6:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 mtima wokonzera ena ziwembu,+ mapazi othamangira kukachita zoipa,+

  • Zekariya 8:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Musamakonzerane ziwembu mumtima mwanu kuti muonetsane tsoka+ ndipo musamakonde kulumbira monama.+ Pakuti zinthu zonsezi ine ndimadana nazo,’+ watero Yehova.”

  • Maliko 7:21
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 21 Pakuti mkatimo, mumtima mwa munthu,+ mumatuluka maganizo oipa. Mumatuluka zadama,*+ zakuba, zaumbanda,+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena