Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Mika 5:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 Dzanja lanu lidzakhala pamwamba pa adani anu,+ ndipo adani anu onse adzaphedwa.”+

  • Zekariya 10:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 Onsewa adzakhala ngati amuna amphamvu+ opondaponda matope a m’misewu ya kunkhondo.+ Iwo adzamenya nkhondo pakuti Yehova ali nawo.+ Adani awo oyenda pamahatchi adzachita manyazi.+

  • Zekariya 12:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 Pa tsiku limenelo, ndidzachititsa mafumu a Yuda kukhala ngati mbaula zamoto pakati pa mitengo,+ komanso ngati miyuni yamoto pamilu ya tirigu wongodula kumene.+ Iwo adzatentha mitundu yonse ya anthu owazungulira, mbali ya kudzanja lamanja ndi kudzanja lamanzere.+ Anthu a mu Yerusalemu adzakhalabe mumzinda wawo wa Yerusalemu.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena