Mateyu 24:13 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 13 Koma amene adzapirire+ mpaka pa mapeto, ndiye amene adzapulumuke.+ Luka 21:36 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 36 Chotero khalani maso+ ndipo muzipemphera mopembedzera+ nthawi zonse, kuti mudzathe kuthawa zinthu zonsezi zimene zikuyembekezeka kuchitika. Kutinso mudzathe kuima pamaso pa Mwana wa munthu.”+
36 Chotero khalani maso+ ndipo muzipemphera mopembedzera+ nthawi zonse, kuti mudzathe kuthawa zinthu zonsezi zimene zikuyembekezeka kuchitika. Kutinso mudzathe kuima pamaso pa Mwana wa munthu.”+