Maliko 6:14 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 14 Tsopano izi zinamveka kwa Mfumu Herode,* chifukwa dzina la Yesu linamveka paliponse. Anthu anali kunena kuti: “Yohane m’batizi wauka kwa akufa, ndipo pa chifukwa chimenechi akuchita ntchito zamphamvu.”+ Luka 9:7 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 7 Tsopano Herode* wolamulira chigawo anamva zonse zimene zinali kuchitika. Iye anathedwa nzeru chifukwa ena anali kunena kuti Yohane anauka kwa akufa.+ Machitidwe 4:27 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 27 Zimenezi zinachitikadi pamene Herode,* Pontiyo Pilato,+ pamodzi ndi anthu a mitundu ina komanso anthu a mu Isiraeli, anasonkhana mumzinda uno ndi kuukira Yesu, mtumiki wanu woyera,+ amene inu munamudzoza.+
14 Tsopano izi zinamveka kwa Mfumu Herode,* chifukwa dzina la Yesu linamveka paliponse. Anthu anali kunena kuti: “Yohane m’batizi wauka kwa akufa, ndipo pa chifukwa chimenechi akuchita ntchito zamphamvu.”+
7 Tsopano Herode* wolamulira chigawo anamva zonse zimene zinali kuchitika. Iye anathedwa nzeru chifukwa ena anali kunena kuti Yohane anauka kwa akufa.+
27 Zimenezi zinachitikadi pamene Herode,* Pontiyo Pilato,+ pamodzi ndi anthu a mitundu ina komanso anthu a mu Isiraeli, anasonkhana mumzinda uno ndi kuukira Yesu, mtumiki wanu woyera,+ amene inu munamudzoza.+