Mateyu 19:29 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 29 Aliyense amene wasiya nyumba, abale, alongo, abambo, amayi, ana kapena minda chifukwa cha dzina langa adzalandira zochuluka kwambiri kuposa zimenezi, ndipo adzapeza moyo wosatha.+ Maliko 10:17 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 17 Tsopano pamene anali kupita, mwamuna wina anam’thamangira ndi kugwada pamaso pake. Kenako anamufunsa kuti: “Mphunzitsi Wabwino, ndichite chiyani kuti ndikapeze moyo wosatha?”+ Luka 10:25 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 25 Kenako munthu wina wodziwa Chilamulo+ anaimirira kuti amuyese. Iye anamufunsa kuti: “Mphunzitsi, ndizichita chiyani kuti ndikapeze moyo wosatha?”+ Luka 18:18 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 18 Tsopano wolamulira wina anamufunsa kuti: “Mphunzitsi Wabwino, ndizichita chiyani kuti ndikapeze moyo wosatha?”+
29 Aliyense amene wasiya nyumba, abale, alongo, abambo, amayi, ana kapena minda chifukwa cha dzina langa adzalandira zochuluka kwambiri kuposa zimenezi, ndipo adzapeza moyo wosatha.+
17 Tsopano pamene anali kupita, mwamuna wina anam’thamangira ndi kugwada pamaso pake. Kenako anamufunsa kuti: “Mphunzitsi Wabwino, ndichite chiyani kuti ndikapeze moyo wosatha?”+
25 Kenako munthu wina wodziwa Chilamulo+ anaimirira kuti amuyese. Iye anamufunsa kuti: “Mphunzitsi, ndizichita chiyani kuti ndikapeze moyo wosatha?”+
18 Tsopano wolamulira wina anamufunsa kuti: “Mphunzitsi Wabwino, ndizichita chiyani kuti ndikapeze moyo wosatha?”+