Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Mateyu 17:23
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 23 ndipo adzamupha. Koma pa tsiku lachitatu adzaukitsidwa.”+ Atamva zimenezi iwo anamva chisoni kwambiri.+

  • Mateyu 28:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 Iye sali pano chifukwa wauka kwa akufa+ monga ananenera. Bwerani muone pamene anagona.

  • Maliko 10:34
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 34 Iwo akam’chitira chipongwe, kum’lavulira, kum’kwapula ndi kumupha, koma patapita masiku atatu, adzauka.”+

  • Luka 18:33
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 33 Akakamaliza kumukwapula+ akamupha,+ koma tsiku lachitatu iye adzauka.”+

  • Machitidwe 10:40
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 40 Ameneyu Mulungu anamuukitsa tsiku lachitatu ndi kumulola kuonekera,+

  • 1 Akorinto 15:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 Ndiponso kuti anaikidwa m’manda,+ kenako anaukitsidwa+ tsiku lachitatu,+ mogwirizana ndi Malemba.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena