Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Maliko 11:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 ndi kuwauza kuti: “Pitani m’mudzi umene mukuuonawo. Mukakalowa mmenemo, mukapeza bulu wamng’ono wamphongo atam’mangirira, amene munthu sanakwerepo chiyambire. Mukam’masule ndi kubwera naye kuno.+

  • Luka 19:30
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 30 Iye anawauza kuti: “Pitani m’mudzi umene mukuuonawo, ndipo mukalowa mmenemo mukapeza bulu wamng’ono wamphongo atamumangirira, amene munthu sanakwerepo chiyambire. Mukamumasule n’kubwera naye kuno.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena