Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Mateyu 16:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 Kodi mfundo yake simukuimvetsabe? Kapena kodi simukukumbukira anthu 5,000 amene anadya mitanda isanu ya mkate, komanso kuchuluka kwa madengu a zotsalira zimene munatolera?+

  • Maliko 3:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 Pamenepo Yesu anawayang’ana mokwiya ndi kumva chisoni kwambiri chifukwa cha kuuma mtima kwawo.+ Kenako anauza munthuyo kuti: “Tambasula dzanja lako.” Iye analitambasuladi, ndipo linakhala labwinobwino.+

  • Maliko 8:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Yesu poona zimenezo, anawafunsa kuti: “N’chifukwa chiyani mukukangana nkhani yosowa mikate?+ Kodi simukuzindikira ndi kumvetsa tanthauzo lake mpaka pano? Kodi mitima yanu ikadali yosazindikira?+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena