Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Mateyu 9:32
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 32 Tsopano pamene iwo anali kunyamuka, anthu anam’bweretsera munthu wosalankhula wogwidwa ndi chiwanda.+

  • Luka 11:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Nthawi inayake anali kutulutsa chiwanda cholepheretsa munthu kulankhula.+ Chiwandacho chitatuluka, munthu wosalankhulayo analankhula, ndipo khamu la anthu linadabwa kwambiri.

  • Machitidwe 9:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 ndipo m’masomphenya waona munthu dzina lake Hananiya, amene anafika ndi kumuika manja kuti ayambenso kuona.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena