Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Mateyu 17:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 Ataona izi, Petulo anauza Yesu kuti: “Ambuye, ndi bwino ife tizikhala pano. Ngati mukufuna, ndimanga mahema atatu pano, limodzi lanu, limodzi la Mose ndi lina la Eliya.”+

  • Luka 9:33
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 33 Tsopano pamene amenewa anali kulekana naye, Petulo anauza Yesu kuti:+ “Mlangizi, ndi bwino kuti ife tizikhala pano. Choncho timange mahema atatu, limodzi lanu, limodzi la Mose ndi lina la Eliya.” Koma iye sanali kuzindikira zimene anali kunena.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena