Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Mateyu 4:24
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 24 Choncho mbiri yake inafalikira mu Siriya+ monse. Anthu anamubweretsera onse amene sanali kumva bwino m’thupi,+ amene anali kuvutika ndi matenda komanso zowawa zamitundumitundu, ogwidwa ndi ziwanda, akhunyu,+ ndi anthu akufa ziwalo, ndipo iye anawachiritsa.

  • Luka 4:40
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 40 Koma pamene dzuwa linali kulowa, onse amene anali ndi anthu odwala matenda osiyanasiyana anawabweretsa kwa iye. Ndipo iye anawachiritsa mwa kuika manja ake pa aliyense.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena