Yesaya 53:9 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 9 Manda ake adzakhala limodzi ndi a anthu oipa,+ ndipo adzakhala limodzi ndi anthu olemera pa imfa yake,+ ngakhale kuti iye sanachite zachiwawa zilizonse+ ndipo m’kamwa mwake munalibe chinyengo.+ Mateyu 27:59 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 59 Yosefe anatenga mtembowo ndi kuukulunga munsalu yoyera yabwino kwambiri,+
9 Manda ake adzakhala limodzi ndi a anthu oipa,+ ndipo adzakhala limodzi ndi anthu olemera pa imfa yake,+ ngakhale kuti iye sanachite zachiwawa zilizonse+ ndipo m’kamwa mwake munalibe chinyengo.+