Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Mateyu 3:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 M’masiku amenewo, Yohane M’batizi+ anapita m’chipululu+ cha Yudeya n’kuyamba kulalikira.

  • Maliko 1:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 Yohane m’batizi anafika m’chipululu, ndipo anali kulalikira za ubatizo monga chizindikiro cha kulapa kuti machimo akhululukidwe.+

  • Luka 1:77
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 77 Kukadziwitsa anthu ake za chipulumutso pokhululukidwa machimo awo,+

  • Machitidwe 13:24
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 24 Mpulumutsi+ ameneyu asanafike, Yohane+ anali atalalikiriratu poyera kwa anthu onse mu Isiraeli za ubatizo, monga chizindikiro cha kulapa.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena