Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Nehemiya 5:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Kuwonjezera apo, ndinakutumula zovala zanga, kenako ndinati: “Mofanana ndi zimenezi, Mulungu woona akutumule munthu aliyense wosachita mogwirizana ndi mawu amenewa, kum’chotsa m’nyumba yake ndi pa zinthu zake zonse. Ndipo munthu wotero akutumulidwe mwa njira imeneyi ndi kukhala wopanda kalikonse.” Pamenepo mpingo wonse unati: “Zikhale momwemo!”*+ Ndipo anayamba kutamanda Yehova.+ Choncho anthuwo anachitadi mogwirizana ndi mawu amenewa.+

  • Mateyu 10:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Kulikonse kumene munthu sakakulandirani kapena kumvetsera mawu anu, potuluka m’nyumba imeneyo kapena mumzinda umenewo sansani fumbi kumapazi anu.+

  • Maliko 6:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Kulikonse kumene sakakulandirani kapena kukumvetserani, pochoka kumeneko sansani fumbi kumapazi anu kuti ukhale umboni kwa iwo.”+

  • Machitidwe 13:51
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 51 Koma Paulo ndi Baranaba anasansira anthuwo fumbi kumapazi awo+ n’kupita ku Ikoniyo.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena