Maliko 6:11 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 11 Kulikonse kumene sakakulandirani kapena kukumvetserani, pochoka kumeneko sansani fumbi kumapazi anu kuti ukhale umboni kwa iwo.”+ Luka 10:6 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 6 Ndipo ngati pakhomopo pali munthu wokonda mtendere, mtendere wanu udzakhala pa iye.+ Koma ngati palibe, udzabwerera kwa inu.+ Luka 10:11 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 11 ‘Ngakhale fumbi la mumzinda wanu uno, limene lamamatira kumapazi kwathu, tikukusansirani.+ Komabe, kumbukirani kuti, ufumu wa Mulungu wayandikira.’ Machitidwe 13:51 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 51 Koma Paulo ndi Baranaba anasansira anthuwo fumbi kumapazi awo+ n’kupita ku Ikoniyo. Machitidwe 18:6 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 6 Koma iwo atapitiriza kumutsutsa ndi kulankhula monyoza,+ iye anakutumula zovala zake+ ndi kuwauza kuti: “Magazi anu+ akhale pamitu panu. Ine ndilibe mlandu.+ Kuyambira tsopano ndizipita kwa anthu a mitundu ina.”+
11 Kulikonse kumene sakakulandirani kapena kukumvetserani, pochoka kumeneko sansani fumbi kumapazi anu kuti ukhale umboni kwa iwo.”+
6 Ndipo ngati pakhomopo pali munthu wokonda mtendere, mtendere wanu udzakhala pa iye.+ Koma ngati palibe, udzabwerera kwa inu.+
11 ‘Ngakhale fumbi la mumzinda wanu uno, limene lamamatira kumapazi kwathu, tikukusansirani.+ Komabe, kumbukirani kuti, ufumu wa Mulungu wayandikira.’
6 Koma iwo atapitiriza kumutsutsa ndi kulankhula monyoza,+ iye anakutumula zovala zake+ ndi kuwauza kuti: “Magazi anu+ akhale pamitu panu. Ine ndilibe mlandu.+ Kuyambira tsopano ndizipita kwa anthu a mitundu ina.”+