Mateyu 9:34 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 34 Koma Afarisi anayamba kunena kuti: “Ameneyu amatulutsa ziwanda ndi mphamvu ya wolamulira ziwanda.”+ Maliko 3:22 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 22 Komanso alembi amene anachokera ku Yerusalemu anali kunena kuti: “Ali ndi Belezebule,* ndipo amatulutsa ziwanda ndi mphamvu ya wolamulira ziwanda.”+
34 Koma Afarisi anayamba kunena kuti: “Ameneyu amatulutsa ziwanda ndi mphamvu ya wolamulira ziwanda.”+
22 Komanso alembi amene anachokera ku Yerusalemu anali kunena kuti: “Ali ndi Belezebule,* ndipo amatulutsa ziwanda ndi mphamvu ya wolamulira ziwanda.”+