Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Habakuku 3:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Ngakhale mkuyu usaphukire maluwa,+ mtengo wa mpesa usabale zipatso, mtengo wa maolivi ulephere kubala zipatso, munda wa m’mphepete mwa phiri usatulutse chakudya,+ nkhosa ndi ng’ombe zithemo m’khola,+

  • Maliko 11:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Ndipo ali chapatali ndithu, anaona mkuyu umene unali ndi masamba. Iye anapita pomwepo kuti akaone ngati angapezemo kanthu. Koma atafika pamtengowo, sanapezemo chilichonse koma masamba okha basi, pakuti sinali nyengo ya nkhuyu.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena