Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ezekieli 34:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 “‘Yehova, Ambuye Wamkulu Koposa, wanena kuti: “Inetu ndidzafunafuna nkhosa zanga ndi kuzisamalira.+

  • Mateyu 18:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 “Mukuganiza bwanji? Ngati munthu ali ndi nkhosa 100 ndipo imodzi mwa nkhosazo n’kusochera,+ kodi sangasiye nkhosa 99 zija m’phiri ndi kupita kukafunafuna yosocherayo?+

  • Luka 19:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Pakuti Mwana wa munthu anabwera kudzafunafuna ndi kupulumutsa anthu osochera.”+

  • 1 Petulo 2:25
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 25 Pakuti munali ngati nkhosa zosochera,+ koma tsopano mwabwerera kwa m’busa+ wanu ndi woyang’anira miyoyo yanu.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena