-
Mateyu 10:12Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
12 Pamene mukulowa m’nyumba, perekani moni kwa a m’banja limenelo.
-
-
Luka 24:36Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
36 Akulankhula choncho Yesu anaimirira pakati pawo [[ndi kuwauza kuti: “Mtendere ukhale nanu.”]]
-