-
Salimo 95:7Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
7 Pakuti iye ndi Mulungu wathu ndipo ife ndife anthu ake. Iye amatisamalira ngati nkhosa zimene akuweta.+
Lero anthu inu mukamvera mawu a Mulungu,+
-
Machitidwe 1:15Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
15 Tsopano m’masiku amenewa, Petulo anaimirira pakati pa abalewo (gulu lonselo linali la anthu pafupifupi 120) n’kunena kuti:
-
-
-