Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yohane 3:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Ndipo palibe munthu amene anakwera kumwamba+ koma Mwana wa munthu+ yekha, amene anatsika kuchokera kumwambako.+

  • Yohane 6:38
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 38 Chifukwa ndinatsika kuchokera kumwamba+ kudzachita chifuniro cha iye amene anandituma, osati chifuniro changa.+

  • Yohane 8:23
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 23 Iye anawauza kuti: “Inu ndinu ochokera pansi pano, ine ndine wochokera kumwamba.+ Inu ndinu ochokera m’dziko lino,+ ine si wochokera m’dziko lino.+

  • Machitidwe 1:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 Atatsiriza kunena zimenezi, Mulungu anamunyamula kupita m’mlengalenga iwo akuonerera,+ ndipo mtambo unamuphimba moti sanathenso kumuona.+

  • Aefeso 4:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Chotero iye anati: “Atakwera kumwamba anagwira anthu ukapolo ndipo anapereka mphatso za amuna.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena