Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Mateyu 15:19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 Mwachitsanzo, maganizo oipa, za kupha anthu, za chigololo, za dama, za kuba, maumboni onama, ndi zonyoza Mulungu,+ zimachokera mumtima.+

  • Luka 22:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Koma Satana analowa mwa Yudasi, wotchedwa Isikariyoti, mmodzi wa ophunzira 12 aja.+

  • Yohane 13:27
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 27 Atamupatsa chidutswa cha mkatecho, pamenepo Satana analowa mwa Yudasi.+ Chotero Yesu anamuuza kuti: “Zimene wakonza kuchita, zichite mwamsanga.”

  • Machitidwe 1:25
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 25 kuti atenge malo a utumiki uwu ndi utumwi,+ amene Yudasi anawasiya ndi kuyenda njira zake.”

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena