Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yohane 12:48
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 48 Aliyense wondinyalanyaza ndi kusalandira mawu anga, ali naye mmodzi womuweruza. Mawu+ amene ine ndalankhula ndi amene adzamuweruze pa tsiku lomaliza.

  • Machitidwe 24:25
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 25 Koma pamene anali kulankhula za chilungamo,+ za kudziletsa,+ ndi za chiweruzo+ chimene chikudzacho, Felike anachita mantha ndipo anayankha kuti: “Basi, padakali pano ungapite, ndikadzapeza nthawi ndidzakuitananso.”

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena