Deuteronomo 29:29 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 29 “Zinthu zobisika+ ndi za Yehova Mulungu wathu, koma zinthu zoululidwa+ ndi zathu ndi ana athu mpaka kalekale, kuti titsatire mawu onse a chilamulo ichi.+ Mateyu 24:36 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 36 “Kunena za tsikulo ndi ola lake,+ palibe amene akudziwa, ngakhale angelo akumwamba kapenanso Mwana, koma Atate yekha.+
29 “Zinthu zobisika+ ndi za Yehova Mulungu wathu, koma zinthu zoululidwa+ ndi zathu ndi ana athu mpaka kalekale, kuti titsatire mawu onse a chilamulo ichi.+
36 “Kunena za tsikulo ndi ola lake,+ palibe amene akudziwa, ngakhale angelo akumwamba kapenanso Mwana, koma Atate yekha.+