Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Numeri 6:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Ndipo apereke kwa Yehova nsembe ya iye mwini. Nsembeyo ikhale nkhosa yaing’ono yamphongo yopanda chilema, yosapitirira chaka chimodzi, monga nsembe yopsereza.+ Aperekenso mwana wa nkhosa wamkazi wopanda chilema, wosapitirira chaka chimodzi, monga nsembe yamachimo.+ Komanso apereke nkhosa yamphongo yopanda chilema, monga nsembe yachiyanjano.+

  • Numeri 6:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Aperekenso dengu la mikate yozungulira yoboola pakati. Mikateyo ikhale yopanda chofufumitsa, yophika ndi ufa wosalala,+ ndi yopaka mafuta.+ M’dengumo mukhalenso timikate topyapyala topanda chofufumitsa topaka mafuta,+ limodzi ndi nsembe yake yambewu,+ ndiponso nsembe zake zachakumwa.+

  • Numeri 6:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Am’perekerenso nkhosa yamphongo monga nsembe yachiyanjano+ kwa Yehova, limodzi ndi dengu la mikate yopanda chofufumitsa ija. Kenako, wansembeyo apereke nsembe yambewu+ ndi nsembe yachakumwa, zimene zimayendera limodzi ndi nsembe yachiyanjanoyo.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena