1 Akorinto 9:1 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 9 Kodi sindine mfulu?+ Kodi sindine mtumwi?+ Kodi sindinaone Yesu Ambuye wathu?+ Kodi inu sindinu ntchito yanga mwa Ambuye? 1 Akorinto 15:8 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 8 Koma pomalizira pake anaonekera kwa ine,+ ngati khanda lobadwa masiku asanakwane.
9 Kodi sindine mfulu?+ Kodi sindine mtumwi?+ Kodi sindinaone Yesu Ambuye wathu?+ Kodi inu sindinu ntchito yanga mwa Ambuye?