Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ezekieli 18:31
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 31 Tayani zolakwa zanu zonse zimene munachita+ ndipo muyesetse kukhala ndi mtima watsopano+ ndiponso mzimu watsopano.+ Kodi muferenji+ inu a nyumba ya Isiraeli?’

  • Mateyu 3:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Ndiyetu mubale zipatso zosonyeza kulapa.+

  • 2 Akorinto 7:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Ndipo taonani zimene chisoni chogwirizana ndi chifuniro cha Mulungu+ chimenechi chakuchitirani. Chakuchititsani kukhala akhama kwambiri, chakuchititsani kudziyeretsa, kuipidwa, mantha, kufunitsitsa kulapa, kudzipereka, ndiponso kukonza cholakwacho.+ Mwanjira ina iliyonse, munasonyeza kuti ndinu oyera pa nkhani imeneyi.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena