Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Mateyu 8:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Choncho anagwira dzanja la mayiwo,+ ndipo malungowo anatheratu, moti anadzuka n’kuyamba kumutumikira.+

  • Yohane 5:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Yesu anati: “Nyamuka, nyamula machira akowa ndi kuyamba kuyenda.”+

  • Machitidwe 9:34
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 34 Ndiyeno Petulo anamuuza kuti:+ “Eneya, Yesu Khristu akukuchiritsa.+ Dzuka ndi kuyala bwino bedi lakoli.” Nthawi yomweyo anadzuka.

  • Machitidwe 14:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Choncho Paulo analankhula mokweza mawu kuti: “Imirira ndi miyendo yako!” Pamenepo iye anadumpha n’kuyamba kuyenda.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena