Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 101:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  7 M’nyumba yanga simudzakhala wochita chinyengo.+

      Ndipo aliyense wolankhula zachinyengo sadzapitiriza kukhala+

      Pamaso panga.+

  • Salimo 119:118
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 118 Onse osochera ndi kuchoka pa malangizo anu mwawataya kutali,+

      Pakuti ndi achinyengo komanso onama.+

  • Aefeso 4:25
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 25 Chotero, popeza tsopano mwataya chinyengo,+ aliyense wa inu alankhule zoona kwa mnzake,+ chifukwa ndife ziwalo za thupi limodzi.+

  • Akolose 3:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 Musamanamizane.+ Vulani umunthu+ wakale pamodzi ndi ntchito zake,

  • Chivumbulutso 21:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Koma amantha, opanda chikhulupiriro,+ odetsedwa amenenso amachita zinthu zonyansa,+ opha anthu,+ adama,+ ochita zamizimu, opembedza mafano,+ ndi onse abodza,+ gawo lawo lidzakhala m’nyanja yoyaka moto+ ndi sulufule.+ Nyanja imeneyi ikuimira imfa yachiwiri.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena