Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Machitidwe 11:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 “Ndinali kupemphera mumzinda wa Yopa. Ndipo ndinayamba kuona masomphenya. M’masomphenyawo ndinaona chinthu chikutsika. Chinthucho chinali chooneka ngati chinsalu chachikulu chimene achigwira m’makona onse anayi, ndipo anali kuchitsitsa kuchokera kumwamba moti chinafika kwa ine.

  • Machitidwe 22:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 “Koma nditabwerera ku Yerusalemu,+ ndipo pamene ndinali kupemphera m’kachisi, ndinayamba kuona masomphenya.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena