Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Genesis 19:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 Ndiyeno anati: “Chonde ambuyanga, patukirani kunyumba ya kapolo wanu. Tikusambitseni mapazi ndiponso mukagone,+ kuti mawa mulawirire n’kupitiriza ulendo wanu.”+ Ndiyeno iwo anati: “Ayi, ife tigona m’bwalo la mzinda usiku wa lero.”+

  • Oweruza 19:20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Koma mwamuna wokalamba uja anati: “Mtendere ukhale nawe!+ Ine ndidzakupatsa chilichonse chimene ungafunikire.+ Koma usagone pabwalo la mzinda.”

  • Luka 24:29
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 29 Koma iwo anamuumiriza kuti: “Tiyeni tikhalebe limodzi, chifukwa kunja kwayamba kuda ndipo tsiku latha kale.” Pamenepo analowa ndi kukakhala nawo.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena