Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Oweruza 19:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 Tsopano mwamunayo+ anaimirira kuti azipita, iyeyo pamodzi ndi mdzakazi wake+ ndiponso mtumiki wake,+ koma apongozi ake, bambo a mtsikanayo, anamuuza kuti: “Anotu ndi madzulo tsopano, ndipo posachedwa kuchita mdima. Chonde, lero mugone kuno.+ Onani, kunja kwatsala pang’ono kuda. Lero mugone kuno ndipo musangalatse mtima wanu.+ Mawa mudzuke m’mawa kwambiri ndi kuyamba ulendo wanu wopita kuhema wanu.”

  • 1 Samueli 29:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Choncho udzuke m’mawa kwambiri pamodzi ndi atumiki a mbuye wako amene anabwera nawe pamodzi. Mukangoona kuti kwayera mudzuke ndi kunyamuka.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena