Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yesaya 1:26
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 26 Ndidzakubweretseraninso oweruza ngati pa chiyambi paja, ndi aphungu ngati poyamba paja.+ Pambuyo pa zimenezi mudzatchedwa Mzinda Wachilungamo ndi Mzinda Wokhulupirika.+

  • Danieli 7:27
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 27 “‘Ufumu, ulamuliro, ndi ulemerero wa maufumu a padziko lonse lapansi zinaperekedwa kwa oyera a Wamkulukulu.+ Ufumu wawo+ udzakhalapo mpaka kalekale ndipo maulamuliro onse adzawatumikira ndi kuwamvera.’+

  • Mika 4:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 “Koma iwe nsanja ya gulu la nkhosa, malo okwera a mwana wamkazi wa Ziyoni,+ ulamuliro udzabwerera kwa iwe. Ulamuliro woyamba, ufumu wa mwana wamkazi wa Yerusalemu,+ udzabwerera kwa iwe.+

  • Luka 19:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Pamene iwo anali kumvetsera zimenezi, iye anawonjezapo fanizo, chifukwa anali pafupi ndi Yerusalemu ndipo anthu anali kuganiza kuti ufumu wa Mulungu uonekera nthawi yomweyo.+

  • Luka 24:21
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 21 Komatu ife tinali kuyembekezera kuti munthu ameneyu ndi amene adzapulumutse Isiraeli.+ Kuwonjezera pamenepo, lero ndi tsiku lachitatu chichitikireni zinthu zimenezi.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena