19 ndipo uyandikire pafupi ndi ana a Amoni. Usawavutitse kapena kumenyana nawo, chifukwa sindidzakupatsa mbali iliyonse ya dziko la ana a Amoni kuti likhale lako. Dziko limeneli ndinalipereka kwa ana a Loti kuti likhale lawo.+
17 Iye ndi amene waziponyera maere, ndipo dzanja lake lazigawira malowo ndi chingwe choyezera.+ Zidzakhala kumeneko mpaka kalekale. Kudzakhala kwawo ku mibadwomibadwo.