1 Akorinto 2:15 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 15 Komano munthu wauzimu+ amafufuza zinthu zonse, koma iye safufuzidwa+ ndi munthu aliyense. Agalatiya 5:22 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 22 Koma makhalidwe* amene mzimu woyera umatulutsa+ ndiwo chikondi, chimwemwe, mtendere, kuleza mtima, kukoma mtima, ubwino,+ chikhulupiriro,
22 Koma makhalidwe* amene mzimu woyera umatulutsa+ ndiwo chikondi, chimwemwe, mtendere, kuleza mtima, kukoma mtima, ubwino,+ chikhulupiriro,