Afilipi 1:11 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 11 Muchite zimenezi kutinso mudzazidwe ndi zipatso zolungama+ kudzera mwa Yesu Khristu, kuti Mulungu akalemekezedwe ndi kutamandidwa.+ Akolose 1:10 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 10 Tikupemphereranso kuti muziyenda mogwirizana ndi zimene Yehova+ amafuna,+ kuti muzimukondweretsa pa chilichonse,+ pamene mukupitiriza kubala zipatso m’ntchito iliyonse yabwino, ndi kuwonjezera kumudziwa Mulungu molondola.+
11 Muchite zimenezi kutinso mudzazidwe ndi zipatso zolungama+ kudzera mwa Yesu Khristu, kuti Mulungu akalemekezedwe ndi kutamandidwa.+
10 Tikupemphereranso kuti muziyenda mogwirizana ndi zimene Yehova+ amafuna,+ kuti muzimukondweretsa pa chilichonse,+ pamene mukupitiriza kubala zipatso m’ntchito iliyonse yabwino, ndi kuwonjezera kumudziwa Mulungu molondola.+