Afilipi 3:11 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 11 Ndachita izi kuti ndiyesetse ndi kuona ngati n’zotheka kudzauka nawo pa kuuka koyambirira+ kuchokera kwa akufa. Chivumbulutso 20:6 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 6 Wodala+ ndi woyera+ ndiye aliyense wouka nawo pa kuuka koyamba. Pa iwo, imfa yachiwiri+ ilibe ulamuliro.+ Koma adzakhala ansembe+ a Mulungu ndi a Khristu, ndipo adzalamulira monga mafumu limodzi naye zaka 1,000.+
11 Ndachita izi kuti ndiyesetse ndi kuona ngati n’zotheka kudzauka nawo pa kuuka koyambirira+ kuchokera kwa akufa.
6 Wodala+ ndi woyera+ ndiye aliyense wouka nawo pa kuuka koyamba. Pa iwo, imfa yachiwiri+ ilibe ulamuliro.+ Koma adzakhala ansembe+ a Mulungu ndi a Khristu, ndipo adzalamulira monga mafumu limodzi naye zaka 1,000.+