Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Aefeso 4:31
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 31 Kuwawidwa mtima konse kwa njiru,+ kupsa mtima, mkwiyo, kulalata ndiponso mawu achipongwe+ zichotsedwe mwa inu limodzi ndi zoipa zonse.+

  • 1 Timoteyo 5:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Komanso pa nthawi yomweyo, amayamba chizolowezi chomangokhala osachita kanthu, n’kumangoyendayenda m’makomo mwa anzawo. Kuwonjezera pa kumangokhala osachita kanthu, amakhalanso amiseche ndi olowerera nkhani za eni,+ n’kumalankhula zimene sayenera kulankhula.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena