Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Machitidwe 18:24
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 24 Tsopano Myuda wina dzina lake Apolo,+ mbadwa ya ku Alekizandiriya, amene anali ndi mphatso ya kulankhula, anafika ku Efeso. Iyeyu analinso kuwadziwa bwino Malemba.+

  • 1 Akorinto 3:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 Ngati wina akunena kuti: “Ine ndine wa Paulo,” ndipo wina akunenanso kuti: “Ine ndine wa Apolo,”+ kodi sindiye kuti mukungofanana ndi anthu onse basi?

  • 1 Akorinto 3:21
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 21 Chotero pasakhale munthu wodzitama chifukwa cha anthu, popeza zinthu zonse ndi zanu,+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena