Salimo 8:6 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 6 Munamupatsa mphamvu kuti alamulire ntchito za manja anu.+Mwaika zonse pansi pa mapazi ake:+ Aefeso 1:22 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 22 Mulungu anaikanso zinthu zonse pansi pa mapazi a iyeyo,+ ndipo anamuika mutu wa zinthu zonse+ chifukwa cha mpingo,
22 Mulungu anaikanso zinthu zonse pansi pa mapazi a iyeyo,+ ndipo anamuika mutu wa zinthu zonse+ chifukwa cha mpingo,