Aroma 8:38 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 38 Pakuti ndatsimikiza mtima kuti imfa, moyo,+ angelo,+ maboma,+ zinthu zimene zilipo, zinthu zimene zikubwera m’tsogolo, mphamvu,+ Afilipi 3:10 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 10 Ndachita zimenezi kuti ndim’dziwe komanso kuti ndidziwe mphamvu ya kuuka kwake kwa akufa.+ Kutinso ndigawane naye m’masautso+ ake, ndi kulolera kufa imfa monga yake.+ 1 Petulo 4:13 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 13 Koma muzikondwera+ pamene mukugawana nawo masautso a Khristu,+ kuti mukasangalalenso ndi kukondwera kwambiri pa nthawi imene ulemerero wake udzaonekere.*+
38 Pakuti ndatsimikiza mtima kuti imfa, moyo,+ angelo,+ maboma,+ zinthu zimene zilipo, zinthu zimene zikubwera m’tsogolo, mphamvu,+
10 Ndachita zimenezi kuti ndim’dziwe komanso kuti ndidziwe mphamvu ya kuuka kwake kwa akufa.+ Kutinso ndigawane naye m’masautso+ ake, ndi kulolera kufa imfa monga yake.+
13 Koma muzikondwera+ pamene mukugawana nawo masautso a Khristu,+ kuti mukasangalalenso ndi kukondwera kwambiri pa nthawi imene ulemerero wake udzaonekere.*+