Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Deuteronomo 2:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 Yehova Mulungu wanu wakudalitsani pa chilichonse chimene dzanja lanu likuchita.+ Iye akudziwa za kuyenda kwanu kudutsa m’chipululu chachikulu ichi. Yehova Mulungu wanu wakhala nanu zaka 40 zimenezi,+ ndipo simunasowe kanthu.”’+

  • 2 Akorinto 9:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Komanso, Mulungu akhoza kuchititsa kuti kukoma mtima kwake konse kwakukulu kusefukire kwa inu. Choncho nthawi zonse mudzakhala ndi zinthu zokwanira kusamalira zosowa zanu, ndipo mudzakhalanso ndi zinthu zambiri zogwiritsa ntchito pa ntchito iliyonse yabwino.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena