Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 73:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  2 Koma ine phazi langa linangotsala pang’ono kupatuka,+

      Mapazi anga anangotsala pang’ono kuterereka.+

  • Aheberi 3:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Chenjerani abale, kuti pakati panu, wina asachoke kwa Mulungu wamoyo n’kukhala ndi mtima woipa wopanda chikhulupiriro.+

  • 2 Petulo 3:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Choncho inu okondedwa, popeza mukudziwiratu zimenezi,+ chenjerani kuti musasochere pokopeka ndi zolakwa za anthu ophwanya malamulowo, kuopera kuti mungalephere kukhala olimba ndipo mungagwe.+

  • Chivumbulutso 2:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 Komabe, ndakupeza ndi mlandu wakuti wasiya chikondi chimene unali nacho poyamba.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena