Mateyu 7:11 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 11 Chotero ngati inuyo, ngakhale kuti ndinu oipa,+ mumadziwa kupereka mphatso zabwino kwa ana anu, kuli bwanji Atate wanu wakumwamba? Ndithudi, iye adzapereka zinthu zabwino+ kwa onse om’pempha! Yohane 3:27 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 27 Poyankha Yohane anati: “Munthu sangalandire kanthu kalikonse akapanda kupatsidwa kuchokera kumwamba.+
11 Chotero ngati inuyo, ngakhale kuti ndinu oipa,+ mumadziwa kupereka mphatso zabwino kwa ana anu, kuli bwanji Atate wanu wakumwamba? Ndithudi, iye adzapereka zinthu zabwino+ kwa onse om’pempha!
27 Poyankha Yohane anati: “Munthu sangalandire kanthu kalikonse akapanda kupatsidwa kuchokera kumwamba.+