Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 29:36, 37
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 36 Uzipereka ngʼombe ya nsembe yamachimo tsiku lililonse kuti iphimbe machimo. Uziyeretsa guwa lansembe ku machimo poliperekera nsembe yophimba machimo, ndipo uzilidzoza kuti likhale loyera.+ 37 Udzatenga masiku 7 poperekera guwa lansembelo nsembe yophimba machimo. Udzaliyeretse kuti likhale guwa lansembe loyera koposa.+ Aliyense wogwira guwa lansembe azikhala woyera.

  • Levitiko 8:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Anawaza ena mwa mafuta odzozerawo maulendo 7 paguwa lansembe nʼkudzoza guwa lansembelo, zipangizo zake zonse, beseni ndi choikapo chake, kuti zikhale zopatulika.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena