Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 27:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 Ndiyeno upange bwalo+ la chihema. Kumbali yakumʼmwera, bwalolo ulitchinge ndi mpanda wa nsalu za ulusi wopota wabwino kwambiri. Mpandawo ukhale mamita 45 mulitali mwake kumbali imodziyo.+

  • Ekisodo 38:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 Ndiyeno anapanga bwalo.+ Kumbali yakumʼmwera ya bwalolo anapangako mpanda wa nsalu za ulusi wopota wabwino kwambiri. Mpandawo unali mamita 45 mulitali mwake.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena