Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 36:35, 36
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 35 Kenako anapanga katani+ ya ulusi wabuluu, ya ubweya wa nkhosa wapepo, ulusi wofiira kwambiri ndi ulusi wopota wabwino kwambiri. Pakataniyo anapetapo+ akerubi.+ 36 Ndiyeno katani imeneyi anaipangira zipilala 4 za mtengo wa mthethe ndipo anazikuta ndi golide. Anapanganso tizitsulo tagolide tokolowekapo katani komanso zitsulo 4 zasiliva zokhazikapo zipilalazo.

  • Luka 23:45
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 45 chifukwa dzuwa linachita mdima. Pa nthawi imeneyi nsalu yotchinga yamʼnyumba yopatulika+ inangʼambika pakati kuchokera pamwamba mpaka pansi.+

  • Aheberi 6:19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 Chiyembekezo chathuchi+ chili ngati nangula* wa miyoyo yathu ndipo nʼchotsimikizika komanso chokhazikika. Chiyembekezochi chimatilowetsa mkati, kuseri kwa katani yotchingira+

  • Aheberi 9:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Koma kuseri kwa nsalu yotchinga yachiwiri+ kunali chipinda chinanso chotchedwa “Malo Oyera Koposa.”+

  • Aheberi 10:19, 20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 Choncho abale, timalimba mtima kulowa mʼmalo oyera+ chifukwa cha magazi a Yesu. 20 Iye ndi amene anatitsegulira njira imeneyi yomwe ndi yatsopano komanso yamoyo ndipo imadutsa katani yotchingira,+ imene ndi thupi lake.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena